< 1 Mbiri 1 >

1 Adamu, Seti, Enosi
Adam, Seth, Enos,
2 Kenani, Mahalaleli, Yaredi,
Cainan, Mahalalel, Jared,
3 Enoki, Metusela, Lameki, Nowa.
Enoch, Methuselah, Lamech,
4 Ana a Nowa, Semu, Hamu ndi Yafeti.
Noah, Shem, Ham, and Japheth.
5 Ana aamuna a Yafeti anali: Gomeri, Magogi, Madai, Yavani, Tubala, Mesaki ndi Tirasi.
The sons of Japheth: Gomer, and Magog, and Madai, and Javan, Tubal, Meshech, Tiras.
6 Ana aamuna a Gomeri anali: Asikenazi, Rifati ndi Togarima
And the sons of Gomer: Ashkenaz, and Riphath, and Togarmah.
7 Ana aamuna a Yavani anali: Elisa, Tarisisi, Kitimu ndi Rodanimu.
And the sons of Javan: Elishah and Tarshish, Kittim and Rodanim.
8 Ana aamuna a Hamu anali: Kusi, Miziraimu, Puti ndi Kanaani
The sons of Ham: Cush, and Mizraim, and Put, and Canaan.
9 Ana aamuna a Kusi anali: Seba, Havila, Sabita, Raama ndi Sabiteka Ana aamuna a Raama anali: Seba ndi Dedani.
And the sons of Cush: Seba, and Havilah, Sabtah, and Raamah, and Sabteca. And the sons of Raamah: Sheba and Dadan.
10 Kusi anali abambo a Nimurodi amene anali wankhondo wamphamvu kwambiri pa dziko lapansi.
Then Cush conceived Nimrod, and he began to be powerful upon the earth.
11 Igupto ndiye kholo la Aludi, Aanami, Alehabu, Anafutu,
Truly, Mizraim conceived Ludim, and Anamim, and Lehabim, and Naphtuhim,
12 Apaturusi, Akasilu (kumene kunachokera Afilisti) ndi Akafitori.
as well as Pathrusim and Casluhim: from these the Philistines and the Caphtorim went forth.
13 Kanaani anabereka mwana wake wachisamba Sidoni, ndipo anaberekanso Ahiti,
Truly, Canaan conceived Sidon, his firstborn, as well as the Hittite,
14 Ayebusi, Aamori, Agirigasi
and the Jebusite, and the Amorite, and the Girgashite,
15 Ahivi, Aariki, Asini
and the Hivite, and the Arkite, and the Sinite,
16 Aaravadi, Azemari ndi Ahamati.
and also the Arvadian, and the Samarite, and the Hamathite.
17 Ana aamuna a Semu anali: Elamu, Asuri, Aripakisadi, Ludi ndi Aramu. Ana aamuna a Aramu anali: Uzi, Huri, Geteri ndi Mesaki.
The sons of Shem: Elam, and Asshur, and Arphaxad, and Lud, and Aram, and Uz, and Hul, and Gether, and Meshech.
18 Aripakisadi anabereka Sela ndipo Selayo anabereka Eberi:
Then Arphaxad conceived Shelah, who also himself conceived Eber.
19 Eberi anabereka ana aamuna awiri: wina anamutcha Pelegi, chifukwa pa nthawiyo anthu a pa dziko lapansi anagawikana. Dzina la mʼbale wake linali Yokitani.
And to Eber were born two sons. The name of one was Peleg, because in his days the earth was divided. And the name of his brother was Joktan.
20 Yokitani anabereka Alimodadi, Selefi, Hazari-Maveti, Yera,
Then Joktan conceived Almodad, and Sheleph, and Hazarmaveth, and Jerah,
21 Hadoramu, Uzali, Dikila
as well as Hadoram, and Uzal, and Diklah,
22 Obali, Abimaeli, Seba,
and then Obal, and Abimael, and Sheba, indeed
23 Ofiri, Havila ndi Yobabu. Onsewa anali ana aamuna a Yokitani.
also Ophir, and Havilah, and Jobab. All these are the sons of Joktan.
24 Semu, Aripakisadi, Sela
Shem, Arphaxad, Shelah,
25 Eberi, Pelegi, Reu
Eber, Peleg, Reu,
26 Serugi, Nahori, Tera
Serug, Nahor, Terah,
27 ndi Abramu (amene ndi Abrahamu).
Abram, the same is Abraham.
28 Ana a Abrahamu ndi awa: Isake ndi Ismaeli.
And the sons of Abraham: Isaac and Ishmael.
29 Zidzukulu zake zinali izi: Nebayoti ndiye anali mwana woyamba wa Ismaeli, kenaka Kedara, Adibeeli, Mibisamu,
And these are their generations: the firstborn of Ishmael, Nebaioth, and then Kedar, and Adbeel, and Mibsam,
30 Misima, Duma, Masa, Hadadi, Tema,
and Mishma, and Dumah, Massa, Hadad, and Tema,
31 Yeturi, Nafisi ndi Kedema. Awa anali ana a Ismaeli.
Jetur, Naphish, Kedemah. These are the sons of Ishmael.
32 Ana a Ketura mzikazi wa Abrahamu anali awa: Zimurani, Yokisani, Medani, Midiyani, Isibaki ndi Suwa. Ana a Yokisani ndi awa: Seba ndi Dedani
And the sons of Keturah, the concubine of Abraham, whom she conceived: Zimran, Jokshan, Medan, Midian, Ishbak, and Shuah. And the sons of Jokshan: Sheba and Dedan. And the sons of Dedan: Asshurim, and Letushim, and Leummim.
33 Ana aamuna a Midiyani anali, Efai, Eferi, Hanoki, Abida ndi Elida. Onsewa anali zidzukulu za Ketura.
And the sons of Midian: Ephah, and Epher, and Hanoch, and Abida, and Eldaah. All these are the sons of Keturah.
34 Abrahamu anabereka Isake. Ana a Isake anali awa: Esau ndi Israeli.
Now Abraham conceived Isaac, whose sons were Esau and Israel.
35 Ana aamuna a Esau anali awa: Elifazi, Reueli, Yeusi, Yolamu ndi Kora.
The sons of Esau: Eliphaz, Reuel, Jeush, Jalam, and Korah.
36 Ana a Elifazi anali awa: Temani, Omari, Zefo, Gatamu ndi Kenazi: Amene anabereka ndi Timna: Amaleki.
The sons of Eliphaz: Teman, Omar, Zepho, Gatam, Kenez, and by Timna, Amalek.
37 Ana a Reueli anali awa: Nahati, Zera, Sama ndi Miza.
The sons of Reuel: Nahath, Zerah, Shammah, Mizzah.
38 Ana a Seiri anali awa: Lotani, Sobala, Zibeoni, Ana, Disoni, Ezeri ndi Disani.
The sons of Seir: Lotan, Shobal, Zibeon, Anah, Dishon, Ezer, Dishan.
39 Ana aamuna a Lotani anali awa: Hori ndi Homamu. Timna anali mlongo wake wa Lotani.
The sons of Lotan: Hori, Heman. Now the sister of Lotan was Timna.
40 Ana aamuna a Sobala anali awa: Alivani, Manahati, Ebala, Sefo ndi Onamu. Ana aamuna a Zibeoni anali awa: Ayiwa ndi Ana.
The sons of Shobal: Alian, and Manahath, and Ebal, Shephi, and Onam. The sons of Zibeon: Aiah and Anah. The sons of Anah: Dishon.
41 Mwana wa Ana anali Disoni. Ana a Disoni anali awa: Hemudani, Esibani, Itirani ndi Kerani
The sons of Dishon: Hamran, and Esheban, and Ithran, and Cheran.
42 Ana aamuna a Ezeri anali awa: Bilihani, Zaavani ndi Yaakani. Ana aamuna a Disani anali awa: Uzi ndi Arani.
The sons of Ezer: Bilhan, and Zaavan, and Akan. The sons of Dishan: Uz and Aran.
43 Awa ndi mafumu amene ankalamulira dziko la Edomu, mfumu iliyonse ya Israeli isanayambe kulamulira kumeneko: Bela mwana wa Beori, mzinda wake ankawutcha Dinihaba.
Now these are the kings who reigned in the land of Edom, before there was a king over the sons of Israel: Bela, the son of Beor; and the name of his city was Dinhabah.
44 Bela atamwalira, Yobabu mwana wa Zera wochokera ku Bozira analowa ufumu mʼmalo mwake.
Then Bela died, and Jobab, the son of Zerah, from Bozrah, reigned in his place.
45 Yobabu atamwalira, Husamu wochokera ku dziko la Atemani, analowa ufumu mʼmalo mwake.
And when Jobab also had died, Husham, from the land of the Temanites, reigned in his place.
46 Husamu atamwalira, Hadadi mwana wa Bedadi, amene anagonjetsa Amidiyani mʼdziko la Mowabu, analowa ufumu mʼmalo mwake. Mzinda wake unkatchedwa Aviti.
Then Husham also passed away, and Hadad, the son of Bedad, reigned in his place. And he struck the Midianites in the land of Moab. The name of his city was Avith.
47 Hadadi atamwalira, Samila wochokera ku Masireka analowa ufumu mʼmalo mwake.
And when Hadad also had died, Samlah from Masrekah reigned in his place.
48 Samila atamwalira, Sauli wochokera ku Rehoboti wa ku Mtsinje analowa ufumu mʼmalo mwake.
Then Samlah also died, and Shaul from Rehoboth, which is situated beside a river, reigned in his place.
49 Sauli atamwalira, Baala-Hanani mwana wa Akibori analowa ufumu mʼmalo mwake.
Shaul also having died, Baal-hanan, the son of Achbor, reigned in his place.
50 Pamene Baala-Hanani anamwalira, Hadadi analowa ufumu mʼmalo mwake. Mzinda wake unkatchedwa Pau, ndipo dzina la mkazi wake linali Mehatabeli mwana wa Matiredi, mwana wamkazi wa Me-Zahabu.
Then he too died, and Hadar reigned in his place. And the name of his city was Pau. And his wife was called Mehetabel, the daughter of Matred, the daughter of Mezahab.
51 Hadadi anamwaliranso. Mafumu a ku Edomu anali: Timna, Aliva, Yeteti,
And Hadar having died, there began to be commanders in Edom in place of kings: commander Thamna, commander Alvah, commander Jetheth,
52 Oholibama, Ela, Pinoni,
commander Oholibamah, commander Elah, commander Pinon,
53 Kenazi, Temani, Mibezari,
commander Kanez, commander Teman, commander Mibzar,
54 Magidieli ndi Iramu. Awa anali mafumu a ku Edomu.
commander Magdiel, commander Iram. These are the commanders of Edom.

< 1 Mbiri 1 >