< Yohane 13 >

1 Inali pafupifupi nthawi ya phwando la Paska. Yesu anadziwa kuti nthawi yafika yoti achoke mʼdziko lapansi ndi kupita kwa Atate. Atawakonda ake amene anali mʼdziko lapansi, Iye anawaonetsa chikondi chake chonse.
Lyahanu pili Mukiti we Paseka niuseni kuliwa Jesu chabezi kuti inakoyakwe chiyasika yakuzwa hanuhansi ni kuya kwa Tayo - sina habakusuni bakwe bamuchisi - ababasaki kutwala kumamanisinzo.
2 Atayamba kudya mgonero, mdierekezi anali atalowa kale mu mtima wa Yudasi Isikarioti mwana wa Simoni, kuti amupereke Yesu.
Lyahanu satani chababiketi kale mwinkulo ya Judasi Iskariota mwana a Simon, kuti abeteke Jesu.
3 Yesu podziwa kuti Atate anamupatsa Iye zonse mʼmanja mwake, ndi kuti Iye anachokera kwa Mulungu ndipo amabwerera kwa Mulunguyo;
Chabakwi kuti Tayo chabahele kale zintu zonso mumayanza akwe imi chabakazwile kwe Ireeza ni chabakubola kwe Ireeza.
4 anayimirira kuchoka pa chakudya navula zovala zake natenga nsalu yopukutira nadzimanga mʼchiwuno mwake.
Abazimani hamulalilo ni kuzwisa chizwanto chakwe chahewulu. Linu chahinda kataulo ni kukalisumina iye mwine.
5 Atachita izi, anathira madzi mʼbeseni ndi kuyamba kusambitsa mapazi a ophunzira ake, ndi kuwapukuta ndi chopukutira chimene anachimanga mʼchiwuno mwake.
Linu chachunka mezi mukasuba ni kutanga kusaza matenda abarutwana bakwe ni kubapemula ni taulo yabalizingelete.
6 Atafika pa Petro, Petroyo anati kwa Iye, “Ambuye, kodi mudzandisambitsa mapazi anga?”
Chakeza kwa Simoni Pitirosi, imi Pitorosi chawamba kwali, “Simwine, mosaze matende angu na?”
7 Yesu anayankha kuti, “Iwe sukuzindikira tsopano chimene ndikuchita, koma udzazindikira mʼtsogolo.”
Jesu chetaba ni chati kwali, “Chinitenda kwanko kese uchizuwisise hanu, kono kokachizuwisise mwinako inza.”
8 Petro anati, “Ayi, Inu simudzandisambitsa konse mapazi anga.” Yesu anayankha kuti, “Ngati Ine sindisambitsa mapazi ako, ulibe gawo mwa Ine.” (aiōn g165)
Pitorosi chawamba kwali, “Kense usanze matende angu.” Jesu chamwitaba, “Heba kanikusazi, kawina chemba kwangu.” (aiōn g165)
9 Simoni Petro anayankha kuti, “Ambuye, osati mapazi okha komanso manja anga ndi mutu wanga womwe!”
Simoni Pitirosi chawamba kwali, “Simwine, kanzi unisazi bulyo kumatende, kono nikumayanza angu ni mutwi wangu.”
10 Yesu anayankha kuti, “Munthu amene wasamba amangofunika kusamba mapazi ake okha chifukwa thupi lake lonse ndi loyera. Ndipo inu ndinu oyera, ngakhale kuti si aliyense mwa inu.”
Jesu chawamba kwali, “Uzo yosazwa kena chasaka, hensi kusazwa kumatende, kono ujolwele neza; ujololwe, kono isini umwi ni umwi.”
11 Pakuti Iye anadziwa amene adzamupereka, ndipo nʼchifukwa chake anati saliyense wa inu ali woyera.
(Mukuti Jesu abezi yese namubeteke; chinji abawambi, “Kahena kutimubonse mujolola.)”
12 Iye atamaliza kusambitsa mapazi awo anavala zovala zake ndi kubwerera pamalo pake. Iye anawafunsa kuti, “Kodi mukuzindikira zimene ndakuchitirani inu?
Linu Jesu hamana kubasaza matende abo ni kuhinda zizwato zakwe ni kwikala hansi hape, chawamba kubali, “Kana mwizi chinatenda kwenu?
13 Inu mumanditcha Ine, ‘Mphunzitsi’ ndi ‘Mbuye,’ ndipo mumakhoza mukamatero, pakuti ichi ndi chimene Ine ndili.
Munisupa 'Muluti' ni 'Simwine,' imi uwamba chishiyeme, kakuti linu njime.
14 Tsono ngati Ine, Mbuye wanu ndi Mphunzitsi wanu, ndasambitsa mapazi anu, inunso muyenera kusambitsana mapazi anu.
Heba njime linu, Simwine ni Muluti, nashanza matende enu, nemwe mulishanze matende enu zumwi ni zumwi.
15 Ine ndakupatsani chitsanzo kuti muzichita monga Ine ndachitira.
Mukuti chinamiha mutala kokuti nenwe mutende bobulyo munamitendela.
16 Zoonadi, Ine ndikukuwuzani kuti wantchito saposa mbuye wake, kapena wotumidwa kuposa amene wamutuma.
Ikumbya line, niwamba kwenu, mubeleki kena mukando kwafumwe; kapa mutumiwa kubamukando kuwamutuma.
17 Ngati inu mudziwa zinthu zimenezi, mudzakhala odala mukamazichita.
Heba nimwiziba izizintu, mufuyoletwe heba nimuzitenda.
18 “Ine sindikunena za inu nonse. Ine ndikudziwa amene ndinawasankha. Koma izi zikukwaniritsa malemba: ‘Iye amene akudya nawo chakudya changa, ndiye amene anandiwukira.’
Kaniwambi mubonse; niziabo banibaketi — kono iñolo linani kwizuzilizwa; 'Iye ulya chikwa changu unilaha mulezele.'
19 “Ine ndikukuwuzani tsopano zisanachitike zimenezi, kuti pamene zachitika, mudzakhulupirire kuti Ine Ndine.
Nimiwambila inzohahanu pili niziseni kutendahala, linukuti hazitendahala, nimuzumine kuti Njime.
20 Zoonadi, Ine ndikukuwuzani kuti aliyense amene alandira amene Ine ndamutuma, alandiranso Ine. Aliyense amene alandira Ine, alandiranso amene anandituma.”
Ikumbya line, nimiwambila, yotambula yese unatuma, watambulame, imi yotambula ime, utambula iye yabanitumi.”
21 Yesu atanena izi, anavutika kwambiri mu mzimu ndipo anachitira umboni kuti, “Zoonadi, Ine ndikukuwuzani kuti mmodzi mwa inu adzandipereka.”
Linu Jesu hawamba inzo, chabakatazehete muluhuho, chaha bupaki mi chati, “Ikumbya line, niwamba kwenu kuti zumwi kwenu kanibeteke.”
22 Ophunzira ake anapenyetsetsana wina ndi mnzake, posadziwa kuti amanena za yani.
Barutwana chibalilola, nibabilelete kuti uwambani.
23 Mmodzi wa ophunzira ake amene Yesu anamukonda, anali atatsamira pachifuwa chake.
Zumwi wabarutwana, wabakusaka hahulu Jesu, abakushendeme hetafule nazendamine hachizuba cha Jesu.
24 Simoni Petro anamukodola wophunzirayo ndi kuti, “Mufunseni akunena za yani.”
Simoni Pitorosi chalolela konzo murutwana ni kuwamba, “Tuwambile njeni unzo yowamba zakwe.”
25 Atamutsamiranso Yesuyo, anamufunsa Iye kuti, “Ambuye, kodi ndani?”
Linu chazendamina hachizuba cha Jesu ni kuwamba kwali, “Simwine, njeni unzo?”
26 Yesu anayankha kuti, “Iye amene ndidzamupatsa buledi amene ndanyema ndikususa ndi ameneyo.” Kenaka, atasunsa gawo la buledi, Iye anapereka kwa Yudasi Isikarioti, mwana wa Simoni.
Linu Jesu chamwitaba, “Njiyena yesenihe chikwa chinansunsa.” Chobulyo hamana kunsunsa chikwa, chachiha Judasi mwana Simon Iskariota.
27 Nthawi yomweyo Yudasi atangodya bulediyo, Satana analowa mwa Iye. Yesu anamuwuza Iye kuti, “Chomwe ukufuna kuchita, chita msanga.”
Imi linu, hakumana chikwa, Satani chamwinjila, linu Jesu chawamba kwali, “Chosakaku tenda, uchitende kakuhwela.”
28 Koma panalibe ndi mmodzi yemwe pa chakudyapo amene anamvetsa chifukwa chimene Yesu ananenera izi kwa iye.
Kakwina nanga umwina kubabalikwikele naye hetafule yabezi kuti chizi hawamba inzo kwali.
29 Popeza Yudasi amasunga ndalama, ena amaganiza kuti Yesu amamuwuza iye kuti akagule zomwe zimafunika pa phwando, kapena kukapereka kanthu kena kake kwa osauka.
Bamwi chiba hupula kuti, mukuti Judasi ibali iye yabakubika masheleni, chingi Jesu abawambi kwali, “Ukawule zisakahala kuti tube nanzo hamukiti,” kapa uwola kukaha zimwi kubanjebwe.
30 Nthawi yomweyo Yudasi atangodya buledi, anatuluka, ndipo unali usiku.
Judasi hamana kutambula chikwa, chazwila hanze hahobulyo. Chi ibali masiku.
31 Yudasi atatuluka, Yesu anati, “Tsopano Mwana wa Munthu walemekezedwa, ndipo mwa Iyeyu Mulungu walemekezedwanso.
Inako Judasi hayenda hanze, Jesu chati, “Hanu Mwana wa Muntu cholumbekwa, imi Ireeza kalumbekwe chebakalyakwe.
32 Ngati Mulungu walemekezedwa mwa Iye, Mulungu mwini adzalemekezanso Mwana, ndipo amulemekeza nthawi yomweyo.
Ireeza kamulumbeke iye kalwake mwine, imi kamulumbeke hahanubulyo.
33 “Ana anga, Ine ndikhala nanu kwa nthawi yochepa chabe. Inu mudzandifunafuna Ine, ndipo monga momwe ndinawawuzira Ayuda, choncho Ine ndikukuwuzani tsopano kuti, kumene Ine ndikupita, inu simungabwereko.
Bahwile banini, nichina nanwe mukuti kuchina kanakozana bulyo. Kamuningane, imi sinamuni bawambili majuda, 'Kuniya kamuwoli kwizako.' Nahanu nichi wamba inzi kwenu hape.
34 “Lamulo latsopano limene ndikukupatsani ndi lakuti: Kondanani wina ndi mnzake, monga momwe Ine ndinakonda inu. Nanunso mukondane wina ndi mnzake.
Nimiha mulao muhya, kuti musake umwi ni umwi; sina munibakumisakila, linu musake umwi ni umwi hape.
35 Mukamakondana aliyense adzadziwa kuti ndinu ophunzira anga.”
Chenzi umwi ni umwi kezibe kuti mubarutwana bangu, heba ni mulisuni zumwi ku zumwi.
36 Simoni Petro anafunsa kuti, “Ambuye, kodi mukupita kuti?” Yesu anayankha kuti, “Kumene Ine ndikupita iwe sunganditsatire tsopano, koma udzanditsatira mʼtsogolo.”
Simoni Pitorosi chawamba kwali, “Simwine, ukaya kuhi?” Jesu abamwitaba, “Kuniya, kowoli kunichilila hanu, kono konichilele inako yiza.”
37 Petro anafunsa kuti, “Ambuye, nʼchifukwa chiyani ine sindingakutsatireni tsopano? Ine ndidzapereka moyo wanga chifukwa cha Inu.”
Pitorosi chati kwali, “Simwine, chinzi hanisawoli kukwichilila? Kanilifungule buhalo bwangu bakeñi chanko.”
38 Kenaka Yesu anayankha kuti, “Kodi iwe udzalolera kutaya moyo chifukwa cha Ine? Zoonadi, Ine ndikukuwuza kuti tambala asanalire, iwe udzandikana katatu!”
Jesu chetaba, “Uwola kulifungula buhalo bwanko ibaka lyangu? Ikumbya line, Nikuwambila, munkombwe niuseni kulila kobe chonisampwile totatwe.”

< Yohane 13 >