< Luka 10 >

1 Zitatha izi Ambuye anasankha enanso 72 ndi kuwatumiza awiriawiri patsogolo pake ku mzinda uliwonse ndi kumalo kumene Iye anatsala pangʼono kupitako.
Pu usikhi ugwa mbombo eyo, Utwa akhanchagula avange “70” nukhuvasuha, vavili vavili vamtalile ukhufikha, ukhu anogwa gwa ukhuluta.
2 Iye anawawuza kuti, “Zokolola ndi zambiri, koma ogwira ntchito ndi ochepa. Pemphani Ambuye wa zokolola, kuti atumize antchito ku munda wake wa zokolola.
Akhavavula, “Uvubeni wingi, lino avavomba mbombo vadebe. Pu tuolove Utwa uvi ibene, pu asuhe nambevi avavomba mbomboavakhubena.
3 Pitani! Ine ndikukutumizani ngati nkhosa pakati pa mimbulu.
Lutaga ikhi lunga kyoni. Mulolage, nikhuvasukha ndi ng'osi pagatinapagati pa Mbwa mwitu.
4 Musatenge chikwama kapena thumba kapena nsapato; ndipo musalonjere wina aliyense pa njira.
Mulugeka upakho ugwa hela, nu pakho ugwa vigenda, na viatu mlekhaga nu khusamusya umunu, munchela.
5 “Mukamalowa mʼnyumba, poyamba nenani kuti, ‘Mtendere pa nyumba ino.’
Munyuba iyakhiva mukwingela mutenchage, ulunonchehencho luvenchage nuve munyumba iyi.'
6 Ngati mʼnyumbamo muli munthu wofuna mtendere, mtendere wanuwo udzakhala pa iyeyo; ngati mulibemo, mtendere wanuwo udzabwerera kwa inu.
Pu umunu angave nu lunonchenchencho iva pwale, ulunonchehencho lwinyo lusigala pamwene lino ingave bakho, lukhilivukha khulyumwe.
7 Khalani mʼnyumba yomweyo, idyani ndi kumwa chilichonse chimene akupatsani, pakuti wantchito ayenera kulandira malipiro ake. Musachoke kumene mwafikirako ndi kupita ku nyumba zina.
Sigalaga munyumba iyo, mulinchage nu khunywa ikhiyakhiva vihumya, ilwakhuva umbombambomba inogiwa ukhupata usahara. Mlahegaga nu khuluta inyumba iyinge.
8 “Mukamalowa mʼmudzi, ndi kulandiridwa, idyani chilichonse akukonzerani.
Uvunjenge uwavenchaga umuyakhiva mukwingila nu khuwapakhela, linchaga kyokyoni ikhuyakhiva vikhuvaletela khumiho agenyo au khundongolo,
9 Chiritsani odwala amene ali kumeneko ndipo muwawuze kuti, ‘Ufumu wa Mulungu wayandikira.’
Ponyaga avatamu avamuvale nukhuvavula. Uvutwa wa, “Nguluve vukwinha vulipipi'
10 Koma mukalowa mʼmudzi ndipo osalandiridwa bwino, kapiteni ku misewu mʼmudzimo nʼkukanena kuti,
Lino imbunjenge uwavenchage umuyakhiva mukwingila nukhusita ukhuvapokhela mlutage khu, namunchila nchovaga,
11 ‘Tikukusansirani ngakhale fumbi la mʼmudzi wanuwu limene lamamatira ku mapazi athuwa. Komabe dziwani izi: Ufumu wa Mulungu wayandikira.’
Utundukhulu imbunchenge wenyo ulyumilile mumalunde gyito tusanyana khulyumwe! Pu mulumanyage, uvutuna wa Nguluve vuhegelile.'
12 Ine ndikuwuzani kuti adzachita chifundo polanga Sodomu pa tsikulo kusiyana ndi mudziwo.
Ni khuvavula ukhuta uvuhigi vuhegulile ukhulutilila khu Sodoma.
13 “Ndiwe watsoka, iwe Korazini! Ndiwe watsoka, iwe Betisaida! Kukanakhala kuti zodabwitsa zimene zinachitika mwa inu zinachitika ku Turo ndi Sidoni, iwo akanatembenuka mtima kale lomwe, atavala ziguduli ndi kudzola phulusa.
Ikyole umwe mwi va Korazini, mwekyale mwi va khu Bethsaida! Ingave imbombo imbaha incha vombikhe mugati indyumwe, yavombeliwe khu Tiro nu Sidoni, vavidova uvusyikhilo ukhuhuma khatale fincho, vagave vitama mugati mumwenda igya magunila ne lyela.
14 Koma adzachita chifundo polanga Turo ndi Sidoni kusiyana ndi inu.
Lino yiva nu khwiyumilincha fincho nu khuhigiwa nu Tiro nu Sidoni fincho numwe.
15 Kodi iwe Kaperenawo, adzakukweza mpaka kumwamba? Ayi, adzakutsitsa mpaka ku Malo a anthu akufa. (Hadēs g86)
Uve vi Kapernamaumu, vusaga ayuvikhugwimekha ukhuluta khukyanya? Bakho, yuvikhukwisya pasi khuvunchukha. (Hadēs g86)
16 “Womvera inu, akumvera Ine; wokana inu, akukana Ine. Ndipo wokana Ine; akukana Iye amene anandituma Ine.”
Mvikhuvapulehyincha umweikhumulihincha une, nu vavnchaga uviyakhiva ukhuvabela ikhumbela vune, nuyakhiva ikhumbela une ambelilyeuviansuhile”
17 Anthu 72 aja anabwerera ndi chimwemwe ndipo anati, “Ambuye, ngakhale ziwanda zinatigonjera ife mʼdzina lanu.”
Avo 70 vakhilikhe nu khuhovokha, puvalikhu nchova, “Utwa, na gamanguluve gikhutwidikhila khulitava lyakho.”
18 Iye anayankha kuti, “Ndinaona Satana akugwa kuchokera kumwamba ngati mphenzi.
Yisu akhavavula akhata, “Nambwene undugu vuigwa ukhuhuma khukyaya ndi enjasi.
19 Ine ndakupatsani ulamuliro woponda njoka ndi zinkhanira, ndi kugonjetsa mphamvu zonse za mdani; palibe chimene chidzakupwetekani.
Lola, nivapile imbombo nu khukhada injokha ne enge, na makha goni nu khu sinda undugu, sa khulikhinu ikhiyakhiva mulemwa khu njila iyo khiyakhiva khikhuvale mauncha.
20 Komabe musakondwere chifukwa mizimu yoyipa inakugonjerani, koma kondwerani chifukwa mayina anu analembedwa kumwamba.”
Lino mlekhe ukhuviginya ukhuta inumbula nyikhuvidikhila, pulino muhovokhsge ingave amatawa ginyo gasimbiwe khukyanya.”
21 Nthawi imeneyo Mzimu Woyera anadzaza Yesu ndi chimwemwe ndipo anati, “Ine ndikulemekeza Inu, Atate Ambuye a kumwamba ndi dziko lapansi, chifukwa mwawabisira anthu anzeru ndi ophunzira zinthu izi ndipo mwaziwulula kwa ana aangʼono. Inde, Atate, pakuti munachita zimenezi mwachifuniro chanu.
Pu uskhi gulagula ahowikhe fincho khu mepo umbalanche, nu khunchova, “Nikhukhugyiniya uve, Dada, Vitwa va khukyanya na pasi pa khilunga, ukhuva ufihile imbombo inchi ukhuhuma khuvanyavulweli nu luhala, nu khugagubatula khu vala avasavimanyisiwa, khuvanaavadebe. Khemene, Dada, ahowikhe khumiho khuvaene.”
22 “Atate anga anapereka zinthu zonse mʼmanja mwanga. Palibe amene amadziwa Mwana kupatula Atate yekha, ndipo palibe amene amadziwa Atate kupatula Mwana yekha, ndiponso amene Mwanayo akufuna kumuwululira.”
Pukhila khinu kyavikhiwwe khulyone nu Dada vango, khisikhu ikyakyumanya umwana viveni nu Dada, pu asikhuli uvikhulumanya u Dada viveni nu mwana. “Nu vyavenchaga, ukhuva umwana ainogwa ukwigubatula khumwene.”
23 Kenaka anatembenukira kwa ophunzira ake nawawuza iwo okha kuti, “Ndi odala maso amene akuona zimene mukuonazi.
Avasyetukhile avakhongi, nu khunchova, khwa khwiyuvilila, “Msayiwe vumukhugavona aga ukhuva umwe, mukhugavona.
24 Pakuti kunena zoona aneneri ambiri ndi mafumu anafunitsitsa kuona zimene mukuonazi koma sanazione, ndi kumva zimene mukumvazi koma sanazimve.”
Nikhuvavula umwe, ukhuta avanyamalago vingi na Vatwa vanogilwe ukhulola imbombo i nchomukhunchivona, pusavanchiwene nu khupulikha, savagapulikhe.”
25 Nthawi ina katswiri wa malamulo anayimirira kuti ayese Yesu. Iye anati, “Aphunzitsi, ndichite chiyani kuti ndikhale ndi moyo wosatha?” (aiōnios g166)
Lola, umanyisi umongi uvandagilo incha khuyahudi avenule nu khugela, akhanchova, akhata, “Imanyisi, negahe ndakhikhi ukhuta nincheningile khuwomi uwasikhu nchoni?” (aiōnios g166)
26 Yesu anayankha kuti, “Mwalembedwa chiyani mʼMalamulo, ndipo iwe umawerenga zotani?”
U Yisu akhambula, “Kyandikhiwe khikhi mululagilo? iyi vukhwimba khikhi?”
27 Iye anayankha kuti, “Uzikonda Yehova Mulungu wako ndi mtima wako wonse, ndi moyo wako wonse, ndi mphamvu zako zonse ndi nzeru zako zonse, ndi kukonda mnansi wako monga iwe mwini.”
Akhanda akhata, “Vukhugana Utwa Unguluve vakho ne numbula yakho yoni, ulwakhuva inumbula yakho yoni, yilinamakha goni nu luhala lwoni nu yunywa mubadihine nu mbili gwakho yuve.”
28 Yesu anayankha kuti, “Iwe wayankha bwino, chita zimenezi ndipo udzakhala ndi moyo.”
U Yisu akhanchova akhanda, “Nu vuyilweli woni. Vomba nde vutamaga.”
29 Koma iye anafuna kudzilungamitsa yekha, ndipo anamufunsanso Yesu kuti, “Kodi mnansi wanga ndani?”
Pu umanyisi, anogwaga ukhwivalila uvuyilweli mwene, Akhambula u Yiau, “Nu uvivabadilikhine iva veni?”
30 Yesu pomuyankha anati, “Munthu wina ankatsikira ku Yeriko kuchokera ku Yerusalemu. Pa njira anavulazidwa ndi achifwamba. Anamuvula zovala zake, namumenya ndi kuthawa, namusiya ali pafupi kufa.
U Yisu akhanda, “Umunu unongi aikhaga ukhuhuma khu Yerusalemu ukhuluta khu Yeriko. Akhangwela pagati pa vanyambuna, vakhapakha ikyuma kyoni nu khutova nu khundekha pu akha pipi nu khufwa.
31 Wansembe ankapita pa njira yomweyo, ndipo ataona munthuyo, analambalala.
Khukhafika usikhi ukuhani aikhaga khu njila yiyiyo, vualolile akhagenda injila iyinge.
32 Chimodzimodzinso, Mlevi wina pamene anafika pa malopo ndi kumuona, analambalalanso.
Na yu Mlawi navope, afikhe pa nchila akhambona vope akhagenda khulukha nji.
33 Koma Msamariya wina, ali pa ulendo wake, anafika pamene panali munthuyo; ndipo atamuona, anamva naye chisoni.
Pu Usamaria yumo, vuigenda munchila, akhambona umunu agatile ilonda ukhufwa, khikhambona ikhisa.
34 Anapita panali munthu wovulalayo, nathira mafuta ndi vinyo pa zilonda zake, nʼkuzimanga. Kenaka anamukweza pa bulu wake, napita naye ku nyumba ya alendo, namusamalira.
Akhahegelela nu khukhunga ifikholo fyamwene nu khubakha imono mufikhoho ne divai pakyanya pa mwene. Akhatoncha pakyanya pa khikhanu kyamwene nu khung'elikha khunyumba iya vahesya nu khundolela.
35 Mmawa mwake anatenga ndalama ziwiri zasiliva nazipereka kwa woyangʼanira nyumbayo, nati, ‘Musamalireni munthuyu, ndipo pobwera ndidzakubwezerani zonse zimene mugwiritse ntchito.’
Isikhuiyikhongile atolile dinali ivili akhapa uviandolelaga nukhumbula, antangaga khukyavenchaga ikhiyakhiva khilutilila ayunihomba vunikhiliwikhe.'
36 “Kodi ukuganiza ndi ndani mwa atatuwa, amene anali mnansi wa munthu amene anavulazidwa ndi achifwambawo?”
Pu veni khuvanu vadatu, uvinubadisine va pa wipi, khumunu uviagwile na vanyambuda’?”
37 Katswiri wa Malamulo uja anayankha kuti, “Amene anamuchitira chifundo.” Yesu anamuwuza kuti, “Pita, uzikachita chimodzimodzi.”
Umanyisi akhanchova akhata, “Vi ula uviavonisye ikisakhu mwene, “U Yisu akhata, “Lutaga ukhavombaga vulevule”
38 Yesu ndi ophunzira ake akuyenda, anafika pa mudzi kumene mayi wotchedwa Marita anamulandira Iye mʼnyumba mwake.
Lino vuvigenga vaingile khu vunjenge, nu dala yumo ilitawa vi Matha amwopilile munyumba iya mwene.
39 Mayiyu anali ndi mchemwali wake wotchedwa Mariya, amene anakhala pa mapazi a Yesu kumverera zimene Iye ankanena.
Ale nu nunave uvialilangiwaga Mariamu, atamile mumalunde ga Ntwa nu phupulihincha ilimenyu lye mwene.
40 Koma Marita anatanganidwa ndi zokonzekera zonse zimene zimayenera kuchitika. Iye anabwera kwa Yesu namufunsa kuti, “Ambuye, kodi simusamala kuti mchemwali wanga wandisiya kuti ndichite ntchito yonse ndekha? Muwuzeni andithandize!”
Lino nu Martha aitwikhile imbombo nchoni incha ukhutelekha ikyakhulya. Alutile khwa Yisu, nu khuta, “Itwa, pusewusaga ukhuta umbaha vango andekhile punivomba? Lino imbule anange imbombo.”
41 Ambuye anati, “Marita, Marita, ukudandaula ndi kuvutika ndi zinthu zambiri,
Pu U Twa akhanda nu khumbula, “Martha, Martha, vukhigatancha khu mbombo inyingi,
42 koma chofunika nʼchimodzi chokha. Mariya wasankha chinthu chabwino, ndipo palibe angamulande chimenechi.”
lino khukhile ikhinu khimo ikhinonu, Mariamu alondile ikhinu ikhinonu, ikhisakhilahega, ukhuhuma khumwene.”

< Luka 10 >