< Masalimo 63 >

1 Salimo la Davide. Pamene anali mʼchipululu cha Yuda. Inu Mulungu, ndinu Mulungu wanga, moona mtima ine ndimakufunafunani; moyo wanga uli ndi ludzu lofuna Inu, thupi langa likulakalaka inu, mʼdziko lowuma ndi lotopetsa kumene kulibe madzi.
Psalm Dawida, gdy przebywał na Pustyni Judzkiej. Boże, ty jesteś moim Bogiem, od rana cię szukam; pragnie ciebie moja dusza, tęskni do ciebie moje ciało w ziemi suchej i spragnionej, [w której] nie ma wody;
2 Inu ndinakuonani ku malo anu opatulika ndipo ndinapenya mphamvu zanu ndi ulemerero wanu.
Abym widział twoją moc i chwałę tak, jak cię ujrzałem w twojej świątyni;
3 Chifukwa chikondi chanu ndi choposa moyo, milomo yanga idzakulemekezani.
Skoro lepsze jest twoje miłosierdzie niż życie, moje wargi będą cię chwaliły;
4 Ndidzakutamandani masiku onse a moyo wanga, ndipo mʼdzina lanu ndidzakweza manja anga.
Tak błogosławić cię będę póki żyję, wzniosę swe ręce w imię twoje.
5 Mudzakhutitsa moyo wanga ndi zonona. Ine ndidzakutamandani ndi mawu anthetemya.
Jak tłuszczem i sadłem będzie nasycona moja dusza, moje usta będą cię wielbić radosnymi wargami;
6 Pa bedi panga ndimakumbukira inu; ndimaganiza za Inu nthawi yonse ya usiku.
Gdy cię wspominam na moim posłaniu i rozmyślam o tobie podczas nocnych straży.
7 Chifukwa ndinu thandizo langa, ine ndimayimba mu mthunzi wa mapiko anu.
Ponieważ byłeś mi pomocą, w cieniu twoich skrzydeł będę się weselił.
8 Moyo wanga umakangamira Inu; dzanja lanu lamanja limandigwiriziza.
Moja dusza przylgnęła do ciebie, twoja prawica mnie podtrzymuje.
9 Iwo amene akufunafuna moyo wanga adzawonongedwa; adzatsikira kunsi kozama kwa dziko lapansi.
Ale ci, którzy dążą do zguby mojej duszy, sami zejdą do głębi ziemi.
10 Iwo adzaperekedwa ku lupanga ndi kukhala chakudya cha ankhandwe.
Będą wydani pod ostrze miecza, staną się łupem lisów.
11 Koma mfumu idzakondwera mwa Mulungu; onse amene amalumbira mʼdzina la Mulungu adzalemekeza Mulunguyo, koma pakamwa pa anthu onama padzatsekedwa.
Lecz król będzie się weselił w Bogu, będzie się chlubił każdy, kto na niego przysięga, a usta kłamców zostaną zamknięte.

< Masalimo 63 >