< Masalimo 82 >

1 Salimo la Asafu. Mulungu akutsogolera msonkhano waukulu; Iye akuweruza pakati pa “milungu.”
Gott steht in der Gemeinde Gottes. Inmitten der Götter wird Er richten.
2 “Mudzateteza osalungama mpaka liti, ndi kukondera anthu oyipa?
Wie lange wollt ihr verkehrt richten und das Angesicht des Ungerechten erheben? (Selah)
3 Tetezani anthu ofowoka ndi amasiye; mukhazikitse ufulu wa anthu osauka ndi ozunzika.
Richtet für den Armen und Waisen; rechtfertigt den Elenden und Darbenden.
4 Landitsani anthu ofowoka ndi osowa; apulumutseni mʼdzanja la anthu oyipa.
Befreit den Armen und Dürftigen, aus der Hand der Ungerechten errettet ihn.
5 “Iwo sadziwa kanthu, sazindikira kalikonse. Amayendayenda mu mdima; maziko onse a dziko lapansi agwedezeka.
Sie erkennen nicht, sie sehen nicht ein, sie wandeln im Finstern, es wanken alle Grundfesten des Landes.
6 “Ndinati, ‘Inu ndinu Mulungu, nonsenu ndinu ana a Wammwambamwamba.’
Ich sagte: Götter seid ihr, und des Allerhöchsten Söhne allesamt.
7 Koma mudzafa ngati anthu wamba; mudzagwa ngati wolamula wina aliyense.”
Doch werdet ihr sterben, wie der Mensch, und wie der Obersten einer werdet ihr fallen.
8 Dzukani Inu Mulungu, weruzani dziko lapansi, pakuti mayiko onse ndi cholowa chanu.
Mache Dich auf, Gott, richte die Erde; denn Du erbst alle Völkerschaften.

< Masalimo 82 >