< Psalm 121 >

1 Ein Stufenlied. - Erhöb ich zu den Bergen meine Augen, von ihrer keinem käm mir Hilfe.
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Ndikweza maso anga ku mapiri; kodi thandizo langa limachokera kuti?
2 Vom Herrn kommt meine Hilfe von dem Schöpfer Himmels und der Erde.
Thandizo langa limachokera kwa Yehova, wolenga kumwamba ndi dziko lapansi.
3 Nie läßt er deine Füße gleiten; dein Hüter schlummert nicht.
Sadzalola kuti phazi lako literereke; Iye amene amakusunga sadzawodzera.
4 O nein! Nicht schläft, nicht schlummert der Hüter Israels.
Taonani, Iye amene amasunga Israeli sadzawodzera kapena kugona.
5 Dein Hüter ist der Herr. Dein Schirm zu deiner Rechten ist der Herr.
Yehova ndiye amene amakusunga; Yehova ndiye mthunzi wako ku dzanja lako lamanja.
6 Dir schadet nicht bei Tag die Sonne und nicht der Mond bei Nacht.
Dzuwa silidzakupweteka nthawi ya masana, kapena mwezi nthawi ya usiku.
7 Vor allem Leid behütet dich der Herr, behütet deine Seele.
Yehova adzakuteteza ku zoyipa zonse; adzasunga moyo wako.
8 Der Herr behütet so dein Kommen wie auch dein Gehn, so jetzt wie alle Zeit.
Yehova adzayangʼanira kutuluka kwako ndi kulowa kwako; kuyambira tsopano mpaka muyaya.

< Psalm 121 >