< Deuteronomio 6 >

1 Ita, dagitoy dagiti bilin, alagaden, ken pangngeddeng nga imbilin ni Yahweh a Diosyo kaniak nga isurok kadakayo, tapno masalimetmetanyo dagitoy iti daga a ballasiwenyo ti Jordan tapno tagikuaenyo;
Awa ndi malamulo, malangizo ndi ziphunzitso zimene Yehova Mulungu wanu anandilamula kuti ndikuphunzitseni kuti mukawatsatire mʼdziko limene mukuwolokera Yorodani kuti mukalitenge,
2 tapno maidayawyo ni Yahweh a Diosyo, tapno masalimetmetanyo dagiti amin nga alagaden ken bilinna nga ibilbilinko kadakayo—dakayo, dagiti annakyo, ken dagiti annak dagiti annakyo, iti amin nga aldaw ti panagbiagyo, tapno mapaatiddug dagiti al-aldawyo.
kuti inuyo, ana anu, ndi zidzukulu zanu mʼtsogolomo mudzaope Yehova Mulungu wanu moyo wanu wonse posunga malangizo ndi malamulo ake onse amene ndinakupatsani inu kuti musangalale ndi moyo wautali.
3 Denggenyo ngarud dagitoy, Israel, ken salimetmetanyo dagitoy, tapno sumayaatkayo, tapno umadukayo unay, iti daga nga agay-ayus ti gatas ken diro, kas iti inkari ni Yahweh a Dios dagiti ammayo nga aramidenna.
Mvera Israeli ndipo usamalitse kuchita malamulowa kuti zinthu zikuyendere bwino mʼdziko ndi kuti muchuluke kwambiri mʼdziko loyenda mkaka ndi uchi monga momwe Yehova Mulungu wa makolo anu anakulonjezerani.
4 Denggenyo, Israel: Maymaysa ni Yahweh a Diostayo.
Tamvani inu Aisraeli, Yehova Mulungu wathu, Yehova ndi mmodzi.
5 Ayatenyo ni Yahweh a Diosyo iti amin a pusoyo, iti amin a kararuayo, ken iti amin a pigsayo.
Uzikonda Yehova Mulungu wako ndi mtima wako wonse, ndi moyo wako wonse, ndi mphamvu zako zonse.
6 Addanto iti pusoyo dagiti sasao nga ibilbilinko kadakayo ita nga aldaw;
Malamulo amene ndakupatsani lero ayenera kukhala mu mtima mwanu.
7 ket siaagawa nga isuroyonto dagitoy kadagiti annakyo; saritaenyo ti maipanggep kadagitoy inton agtugawkayo iti uneg ti balayyo, inton magnakayo iti dalan, inton agiddakayo, ken inton bumangonkayo.
Muziwaphunzitsa mwachangu kwa ana anu. Muzikamba za malamulowa pamene muli mʼnyumba zanu, pamene mukuyenda mʼnjira, pamene mukugona ndi pamene mukudzuka.
8 Igalutyonto dagitoy a kas pagilasinan iti imayo, ken agserbidanto a kas pannakabedbed iti nagbaetan dagiti matayo.
Muwamange ngati zizindikiro pa manja anu ndi kuwamangirira pa zipumi zanu.
9 Isuratyonto dagitoy kadagiti poste ti ridaw ti balayyo ken kadagiti ruanganyo.
Muwalembe pa mphuthu za nyumba zanu ndi pa zipata zanu.
10 Inton ipannakayo ni Yahweh a Diosyo iti daga nga insapatana kadagiti ammayo, kada Abraham, Isaac, ken ni Jacob, nga itedna kadakayo, nga addaan kadagiti dadakkel ken nasayaat unay a siudad a saanyo nga impatakder,
Pamene Yehova Mulungu wanu akukulowetsani ndi kukupatsani dziko limene analumbirira makolo anu Abrahamu, Isake ndi Yakobo, dziko lokhala ndi mizinda ikuluikulu imene inu simunamange,
11 ken balbalay a napno kadagiti amin a kita dagiti nasayaat a banbanag a saanyo nga inaramid, kadagiti bubon a saanyo a kinali, ken kadagiti kaubasan ken olibo a kaykayo a saanyo nga inmula, mangankayonto ket mapnekkayo—
nyumba zodzaza ndi zinthu za mitundu yonse zimene inu simunayikemo, zitsime zimene inu simunakumbe, minda ya mpesa ndi mitengo ya olivi zimene inuyo simunadzale, tsono mukadya ndi kukhuta,
12 agannadkayo ngarud tapno saanyo a malipatan ni Yahweh, a nangiruar kadakayo iti daga ti Egipto, iti balay ti pannakaadipen.
samalani kuti mungayiwale Yehova amene anakutulutsani ku Igupto, kukuchotsani mu ukapolo.
13 Dayawenyo ni Yahweh a Diosyo; isuna ti pagrukbabanyo, ken agsapatakayo babaen iti naganna.
Muziopa Yehova Mulungu wanu ndi kumutumikira Iye yekha, ndipo muzilumbira pa dzina lake.
14 Dikay sumurot kadagiti sabali a dios, dagiti dios dagiti tattao nga adda iti aglawlawyo—
Musamatsatire milungu ina, milungu ya anthu ena okuzungulirani,
15 ta ni Yahweh a Diosyo nga adda iti tengngayo ket managimon a Dios—amangan no sumged ti pungtot ni Yahweh a Diosyo a maibusor kadakayo ket dadaelennakayo iti rabaw ti daga.
pakuti Yehova Mulungu wanu amene ali pakati panu, ndi Mulungu wansanje ndipo adzakukwiyirani kwambiri ndi kukuwonongani, kukufafanizani mʼdziko.
16 Diyo suboken ni Yahweh a Diosyo a kas iti panangsubokyo kenkuana idiay Massa.
Musamuyese Yehova Mulungu wanu monga munachitira ku Masa.
17 Siaagawa a salimetmetanyonto dagiti bilin ni Yahweh a Diosyo, dagiti pammaneknekna, ken dagiti alagadenna, nga imbilinna kadakayo.
Onetsetsani kuti mukusunga malamulo a Yehova Mulungu wanu, malangizo ake ndi zikhazikitso zake zimene anakulamulirani.
18 Aramidenyo ti nalinteg ken nasayaat iti imatang ni Yahweh, tapno sumayaatkayo, ken tapno maserrek ken matagikuayo ti nadam-eg a daga nga inkari ni Yahweh kadagiti ammayo,
Chitani zoyenera ndi zabwino pamaso pa Yehova, kuti zikuyendereni bwino ndi kuti mukhoza kukalowa ndi kulanda dziko labwinolo limene Yehova analonjeza molumbira kwa makolo anu,
19 a pagtalawenna dagiti amin a kabusoryo iti sangoananyo, a kas iti imbaga ni Yahweh.
kupirikitsiratu adani anu onse, monga Yehova wanenera.
20 Inton saludsoden kadakayo ti anakyo iti tiempo nga umay, a kunana, 'Ania ti kayat a sawen dagitoy a banbanag—dagiti pammaneknek, dagiti alagaden, ken dagiti dadduma a pangngeddeng nga imbilin ni Yahweh a Diostayo kadakayo?'
Mʼtsogolo muno, ana anu akadzakufunsani kuti, “Kodi tanthauzo la ndondomeko, malangizo, zikhazikitso ndi malamulo amene Yehova Mulungu wathu anakulamulani nʼchiyani?”
21 ket kunayonto iti anakyo, 'Tagabunakami idi ni Faraon idiay Egipto; inruarnakami ni Yahweh idiay Egipto babaen iti nabileg nga imana,
Inu mudzawawuze kuti, “Ife tinali akapolo a Farao ku Igupto, koma Yehova anatitulutsa ku Igupto ndi dzanja lamphamvu.
22 ken nangipakita isuna kadagiti pagilasinan ken nakaskasdaaw, dakkel ken makadidigra, iti Egipto, kenni Faraon, ken iti amin a balayna, iti sangoanan dagiti matatayo;
Ifeyo tikuona Yehova anatumiza zizindikiro zozizwitsa ndi zodabwitsa, zazikulu ndi zoopsa, pa Aigupto ndi Farao pamodzi ndi banja lake lonse.
23 ken inruarnatayo sadiay, tapno maipannatayo, tapno itedna kadatayo ti daga nga inkarina kadagiti ammatayo.
Koma anatitulutsa kumeneko ndi kutilowetsa kuno natipatsa dziko limene analonjeza mwa lumbiro kwa makolo athu.
24 Imbilin ni Yahweh kadatayo a kanayontayo a salimetmetan amin dagitoy nga alagaden, tapno agbutengtayo kenkuana a Diostayo para iti pagsayaatantayo, tapno taginayonennatayo a biagen, a kas kadatayo iti daytoy nga aldaw.
Yehova anatilamula kuti tizimvera malamulo onsewa, kuti tizimuopa kuti zinthu zizitiyendera bwino pa moyo wathu monga momwe zilili leromu.
25 No salimetmetantayo amin dagitoy a bilin iti sangoanan ni Yahweh a Diostayo, kas iti imbilinna kadatayo, daytoyto ti kinalintegtayo.
Ndipo ngati tisamala kumvera malamulo onsewa pamaso pa Yehova Mulungu wathu monga momwe anatilamulira ife, chimenecho chidzakhala chilungamo chathu.”

< Deuteronomio 6 >