< 1 Cronache 9 >

1 COSÌ tutti gl'Israeliti furono annoverati per le lor generazioni; ed ecco, sono descritti nel libro dei re d'Israele. Ora, dopo che que' di Giuda furono stati menati in cattività in Babilonia, per li lor misfatti;
Aisraeli onse analembedwa potsata mibado yawo mʼbuku la mafumu a Aisraeli. Anthu a ku Yuda anatengedwa kunka ku ukapolo ku Babuloni chifukwa cha kusakhulupirika kwawo.
2 e che i primieri abitatori, ch'[erano] altre volte dimorati nelle lor possessioni, furono ritornati nelle lor città: Israeliti, sacerdoti, Leviti, e Netinei;
Tsono anthu oyamba kukhala mʼmadera awo anali Aisraeli wamba, ansembe, Alevi ndi otumikira ku Nyumba ya Yehova.
3 in Gerusalemme abitarono dei figliuoli di Giuda, e de' figliuoli di Beniamino, e de' figliuoli di Efraim e di Manasse:
Anthu a ku Yuda, Benjamini ndi Efereimu ndiponso Manase amene anakhala mu Yerusalemu anali awa:
4 Utai, figliuolo di Ammihud, figliuolo di Omri, figliuolo d'Imri, figliuolo di Bani, de' figliuoli di Fares, figliuolo di Giuda.
Utai mwana wa Amihudi, mwana wa Omuri, mwana wa Imuri, mwana wa Bani, chidzukulu cha Perezi mwana wa Yuda.
5 E de' Siloniti: Asaia il primogenito, ed i suoi figliuoli.
A banja la Siloni: Asaya mwana wake woyamba pamodzi ndi ana ake.
6 E de' figliuoli di Zara: Ieuel, ed i suoi fratelli [in numero di] seicennovanta.
A banja la Zera: Yeueli. Anthu ochokera ku Yuda analipo 690.
7 E de' figliuoli di Beniamino: Sallu, figliuolo di Mesullam, figliuolo di Hodavia, figliuolo di Hassenua;
A fuko la Benjamini: Salu mwana wa Mesulamu, mwana wa Hodaviya, mwana wa Hasenuya;
8 ed Ibnea, figliuolo di Ieroham, ed Ela, figliuolo di Uzzi, figliuolo di Micri; e Mesullam, figliuolo di Sefatia, figliuolo di Reuel, figliuolo d'Ibnia;
Ibineya mwana wa Yerohamu; Ela mwana wa Uzi, mwana wa Mikiri; ndi Mesulamu mwana wa Sefatiya, mwana wa Reueli mwana wa Ibiniya.
9 ed i lor fratelli, [spartiti] per le lor generazioni, [in numero di] novecencinquantasei; tutti coloro [furono] capi di [famiglie] paterne della casa de' lor padri.
Anthu ochokera ku Benjamini monga analembedwera mwa mibado yawo, analipo 956. Anthu onsewa anali atsogoleri a mabanja awo.
10 E de' sacerdoti: Iedaia, e Ioiarib, e Iachin;
Ansembe: Yedaya, Yehoyaribu; Yakini;
11 ed Azaria, figliuolo d'Hilchia, figliuolo di Mesullam, figliuolo di Sadoc, figliuolo di Meraiot, figliuolo di Ahitub, conduttore della Casa di Dio.
Azariya mwana wa Hilikiya, mwana wa Mesulamu, mwana wa Zadoki mwana wa Merayoti, mwana wa Ahitubi, wamkulu woyangʼanira Nyumba ya Mulungu;
12 Ed Adaia, figliuolo di Ieroham, figliuolo di Pashur, figliuolo di Malchia; e Masai, figliuolo di Adiel, figliuolo di Iazera, figliuolo di Mesullam, figliuolo di Messillemit, figliuolo d'Immer;
Adaya mwana wa Yerohamu, mwana wa Pasi-Huri, mwana wa Malikiya; ndi Maasai mwana wa Adieli, mwana wa Yahizera, mwana wa Mesulamu, mwana wa Mesilemoti, mwana wa Imeri.
13 co' lor fratelli, capi delle lor famiglie paterne, [in numero di] millesettecensessanta, [uomini] prodi e valenti, [per] l'opera del servigio della Casa di Dio.
Ansembe amene anali atsogoleri a mabanja awo analipo 1,760. Anali anthu amphamvu ndi odziwa kutumikira mʼnyumba ya Mulungu.
14 E de' Leviti: Semaia, figliuolo di Hassub, figliuolo di Azricam, figliuolo di Hasabia, de' figliuoli di Merari.
Alevi: Semaya mwana wa Hasubu, mwana wa Azirikamu, mwana wa Hasabiya, wa mʼbanja la Merari;
15 E Bacbaccar, ed Heres, e Galal, e Mattania, figliuolo di Mica, figliuolo di Zicri, figliuolo di Asaf;
Bakibakara, Heresi, Galali ndi Mataniya mwana wa Mika, mwana wa Zikiri, mwana wa Asafu;
16 ed Obaidia, figliuolo di Semaia, figliuolo di Galal, figliuolo di Iedutun; e Berechia, figliuolo di Asa, figliuolo di Elcana, il quale abitò nelle villate de' Netofatiti.
Obadiya mwana wa Semaya mwana wa Galali, mwana wa Yedutuni ndi Berekiya mwana wa Asa, mwana wa Elikana, amene ankakhala ku midzi ya Anetofati.
17 E de' portinai: Sallum, ed Accub, e Talmon, ed Ahiman, co' lor fratelli, [dei quali fu] capo Sallum;
Alonda a pa makomo: Salumu, Akubu, Talimoni, Ahimani ndi abale awo. Mtsogoleri wawo anali Salumu.
18 e [lo è] infino ad ora, ed [ha la guardia] della porta del re, verso Oriente; costoro [furono] portinai, fra le schiere de' figliuoli di Levi;
Amenewa amakhala pa chipata cha mfumu kummawa mpaka lero lino. Alonda a gulu la Alevi anali awa:
19 come Sallum, figliuolo di Core, figliuolo di Ebiasaf, figliuolo di Core, ed i suoi fratelli Coriti, della casa paterna di esso, nell'opera del ministerio [erano stati] guardiani della soglia del Tabernacolo; come i lor padri nel campo del Signore, [erano stati] guardiani dell'entrata;
Salumu mwana wa Kore, mwana wa Ebiyasafu, mwana wa Kora, pamodzi ndi abale ake a ku banja la makolo ake, Akora aja ankanyangʼanira khomo la Tenti monga ankachitira abambo awo polondera khomo la malo okhalapo Yehova.
20 e Finees, figliuolo di Eleazaro, col quale il Signore [era], anticamente era stato conduttore sopra loro;
Masiku oyamba Finehasi mwana wa Eliezara anali woyangʼanira alonda apakhomo ndipo Yehova anali naye.
21 [e come] Zaccaria, figliuolo di Meselemia, [era stato] portinaio dell'entrata del Tabernacolo della convenenza.
Zekariya mwana wa Meselemiya anali mlonda woyangʼanira pa chipata cha tenti ya msonkhano.
22 Tutti questi [sono] quelli che [furono] scelti per portinai nelle soglie, [in numero di] dugento dodici. Essi furono annoverati per le lor generazioni nelle lor villate. ([Or] Davide, e il veggente Samuele, li aveano stabiliti nell'ufficio loro.)
Onse amene anasankhidwa kukhala alonda pa khonde analipo 212. Iwo analembedwa mwa mibado yawo ku midzi yawo. Davide ndi mneneri Samueli ndiwo anawayika mʼmalo awo antchito chifukwa cha kukhulupirika kwawo.
23 Ed essi, e i lor figliuoli, [erano costituiti] sopra le porte della Casa del Signore, della Casa del Tabernacolo, per [far] la guardia a vicenda.
Iwo ndi zidzukulu zawo anali oyangʼanira zipata za nyumba ya Yehova imene imatchedwa Tenti.
24 I portinai erano disposti per li quattro venti: dall'Oriente, dall'Occidente, dal Settentrione, e dal Mezzodì.
Alonda apakhomowa anali mbali zonse zinayi: kummawa, kumadzulo, kumpoto ndi kummwera.
25 E i lor fratelli, [ch'erano] nelle lor villate, [aveano] da venire a [dimorar] con essi per sette giorni, di tempo in tempo.
Abale awo a ku midzi yawo amabwera nthawi ndi nthawi kudzagwira ntchito yawo kwa masiku asanu ndi awiri.
26 Perciocchè quei quattro maggiori portinai Leviti [erano] del continuo in ufficio, ed aveano la cura delle camere, e tesori della Casa di Dio.
Koma atsogoleri akuluakulu anayi a alonda, amene anali Alevi, anapatsidwa udindo woyangʼanira zipinda ndi chuma cha nyumba ya Mulungu.
27 E giacevano la notte intorno alla Casa di Dio; perciocchè la guardia ne era loro imposta, ed aveano il carico di aprirla ogni mattina.
Iwo amakhala usiku wonse atayima mozungulira Nyumba ya Mulungu, chifukwa anayenera kuyilondera. Ndipo anali ndi kiyi wotsekulira mmawa uliwonse.
28 Ed [alcuni] di loro aveano la cura dei vasellamenti del servigio; perciocchè si portavano dentro a conto, e si traevano [altresì] fuori a conto.
Ena amayangʼanira zipangizo zimene amagwiritsa ntchito pa ntchito mʼNyumba ya Mulungu. Iwo amaziwerenga zikamalowetsedwa ndi potulutsidwa.
29 Ed [altri] di loro erano costituiti sopra le [altre] masserizie, e sopra tutti gli arredi sacri, e sopra il fior della farina, e sopra il vino, e sopra l' olio, e sopra l'incenso, e sopra gli aromati.
Ena anapatsidwa udindo wosamalira zipangizo ndi zinthu zina zonse za ku malo opatulika, pamodzi ndi ufa, vinyo, mafuta, lubani ndi zonunkhira.
30 Ma quelli che componevano il profumo degli aromati, [erano] de' figliuoli de' sacerdoti.
Koma ansembe ena amasakaniza zonunkhirazo.
31 E d'infra i Leviti, Mattitia, primogenito di Sallum, Corita, avea il carico di ciò che si coceva in su la tegghia.
Mlevi wotchedwa Matitiya mwana woyamba wa Salumu wa mʼbanja la Kora, anapatsidwa udindo woyangʼanira zophikidwa mʼziwaya.
32 E d'infra i lor fratelli, figliuoli de' Chehatiti, alcuni aveano la cura de' pani disposti per ordine, per apparecchiarli ogni sabato.
Abale ake ena a mʼbanja la Akohati amaphika buledi wa pa Sabata lililonse amene amayikidwa pa tebulo.
33 Altri eziandio [erano] cantori, capi di [famiglie] paterne de' Leviti, [i quali stavano] nelle camere, esenti [d'altra cura]; perciocchè l'ufficio loro richiedeva che fossero giorno e notte in opera.
Atsogoleri a mabanja a Alevi, amene anali ndi luso loyimba, amakhala mʼzipinda za Nyumba ya Mulungu ndipo samagwira ntchito zina chifukwa ankatumikira usana ndi usiku.
34 Questi [furono] i capi delle [famiglie] paterne dei Leviti, capi delle lor generazioni. Essi abitarono in Gerusalemme.
Onsewa anali atsogoleri a mabanja a Alevi, akuluakulu monga analembedwera pa mibado yawo, ndipo ankakhala mu Yerusalemu.
35 Or in Gabaon abitò Ieiel, padre di Gabaon; ed il nome della sua moglie [era] Maaca.
Yeiyeli abambo a Gibiyoni ankakhala ku Gibiyoni. Dzina la akazi awo linali Maaka,
36 E il suo figliuolo primogenito [fu] Abdon; poi [ebbe] Sur, e Chis,
ndipo mwana wawo woyamba kubadwa anali Abidoni, motsatana ndi Zuri, Kisi, Baala, Neri, Nadabu,
37 e Baal, e Ner, e Nadab, e Ghedor, ed Ahio, e Zaccaria, e Miclot.
Gedori, Ahiyo, Zekariya ndi Mikiloti.
38 E Miclot generò Simeam; ed essi abitarono dirimpetto ai lor fratelli in Gerusalemme, co' lor fratelli.
Mikiloti anabereka Simeamu. Iwonso ankakhala ndi abale awo ku Yerusalemu.
39 E Ner generò Chis, e Chis generò Saulle, e Saulle generò Gionatan, e Malchi-sua, ed Abinadab, ed Esbaal.
Neri anabereka Kisi, Kisi anabereka Sauli, ndipo Sauli anabereka Yonatani, Maliki-Suwa, Abinadabu ndi Esibaala.
40 E il figliuolo di Gionatan [fu] Merib-baal; e Merib-baal generò Mica.
Mwana wa Yonatani anali Meri-Baala, amene anabereka Mika.
41 Ed i figliuoli di Mica [furono] Piton, e Melec, e Tarea, ed Achaz,
Ana a Mika anali: Pitoni, Meleki, Tahireya ndi Ahazi.
42 [il quale] generò Iara. E Iara generò Alemet, ed Azmavet, e Zimri; e Zimri generò Mosa.
Ahazi anabereka Yara, Yara anabereka Alemeti, Azimaveti ndi Zimuri, ndipo Zimiri anabereka Moza.
43 E Mosa generò Bina, di cui [fu] figliuolo Refaia, di cui [fu] figliuolo Elasa, di cui [fu] figliuolo Asel.
Moza anabereka Bineya. Ana ake anali Refaya, Eleasa ndi Azeli.
44 Ed Asel ebbe sei figliuoli, i cui nomi [sono: ] Azricam, e Bocru, ed Ismaele, e Searia, ed Obadia, ed Hanan. Questi [furono] i figliuoli di Asel.
Azeli anali ndi ana asanu ndi mmodzi ndipo mayina awo anali awa: Azirikamu, Bokeru, Ismaeli, Seariya, Obadiya ndi Hanani. Awa anali ana a Azeli.

< 1 Cronache 9 >