< 歴代誌Ⅰ 1 >

1 アダム、セツ、エノス
Adamu, Seti, Enosi
2 ケナン、マハラレル、ヤレド
Kenani, Mahalaleli, Yaredi,
3 エノク、メトセラ、ラメク
Enoki, Metusela, Lameki, Nowa.
4 ノア、セム、ハム、ヤペテ
Ana a Nowa, Semu, Hamu ndi Yafeti.
5 ヤベテの子等はゴメル、マゴグ、マデア、ヤワン、トバル、メセク、テラス
Ana aamuna a Yafeti anali: Gomeri, Magogi, Madai, Yavani, Tubala, Mesaki ndi Tirasi.
6 ゴメルの子等はアシケナズ、リパテ、トガルマ
Ana aamuna a Gomeri anali: Asikenazi, Rifati ndi Togarima
7 ヤワンの子等はエリシヤ、タルシシ、キツテム、ドダニム
Ana aamuna a Yavani anali: Elisa, Tarisisi, Kitimu ndi Rodanimu.
8 ハムの子等はクシ、ミツライム、プテ、カナン
Ana aamuna a Hamu anali: Kusi, Miziraimu, Puti ndi Kanaani
9 クシの子等はセバ、ハビラ、サブタ、ラアマ、サブテカ、ラアマの子等はセバとデダン
Ana aamuna a Kusi anali: Seba, Havila, Sabita, Raama ndi Sabiteka Ana aamuna a Raama anali: Seba ndi Dedani.
10 クシ、ニムロデを生り彼はじめて世の權力ある者となれり
Kusi anali abambo a Nimurodi amene anali wankhondo wamphamvu kwambiri pa dziko lapansi.
11 ミツライムはルデ族アナミ族レハビ族ナフト族
Igupto ndiye kholo la Aludi, Aanami, Alehabu, Anafutu,
12 パテロス族カスル族カフトリ族を生りカスル族よりペリシテ族出たり
Apaturusi, Akasilu (kumene kunachokera Afilisti) ndi Akafitori.
13 カナンその冢子シドンおよびヘテを生み
Kanaani anabereka mwana wake wachisamba Sidoni, ndipo anaberekanso Ahiti,
14 またヱブス族アモリ族ギルガシ族
Ayebusi, Aamori, Agirigasi
15 ヒビ族アルキ族セニ族
Ahivi, Aariki, Asini
16 アルワデ族ゼマリ族ハマテ族を生り
Aaravadi, Azemari ndi Ahamati.
17 セムの子等はエラム、アシユル、アルバクサデ、ルデ、アラム、ウズ、ホル、ゲテル、メセク
Ana aamuna a Semu anali: Elamu, Asuri, Aripakisadi, Ludi ndi Aramu. Ana aamuna a Aramu anali: Uzi, Huri, Geteri ndi Mesaki.
18 アルバクサデ、シラを生みシラ、エベルを生り
Aripakisadi anabereka Sela ndipo Selayo anabereka Eberi:
19 エベルに二人の子生れたりその一人の名をベレグ(分)と曰ふ其は彼の代に地の人散り分れたればなりその弟の名をヨクタンと曰ふ
Eberi anabereka ana aamuna awiri: wina anamutcha Pelegi, chifukwa pa nthawiyo anthu a pa dziko lapansi anagawikana. Dzina la mʼbale wake linali Yokitani.
20 ヨクタンはアルモダデ、シヤレフ、ハザルマウテ、ヱラ
Yokitani anabereka Alimodadi, Selefi, Hazari-Maveti, Yera,
21 ハドラム、ウザル、デクラ
Hadoramu, Uzali, Dikila
22 エバル、アビマエル、シバ
Obali, Abimaeli, Seba,
23 オフル、ハビラおよびヨハブを生り是等はみなヨクタンの子なり
Ofiri, Havila ndi Yobabu. Onsewa anali ana aamuna a Yokitani.
24 セム、アルバクサデ、シラ
Semu, Aripakisadi, Sela
25 エベル、ベレグ、リウ
Eberi, Pelegi, Reu
26 セルグ、ナホル、テラ
Serugi, Nahori, Tera
27 アブラム是すなはちアブラハムなり
ndi Abramu (amene ndi Abrahamu).
28 アブラハムの子等はイサクおよびイシマエル
Ana a Abrahamu ndi awa: Isake ndi Ismaeli.
29 彼らの子孫は左のごとしイシマエルの冢子はネバヨテ次はケダル、アデビエル、ミブサム
Zidzukulu zake zinali izi: Nebayoti ndiye anali mwana woyamba wa Ismaeli, kenaka Kedara, Adibeeli, Mibisamu,
30 ミシマ、ドマ、マツサ、ハダデ、テマ
Misima, Duma, Masa, Hadadi, Tema,
31 ヱトル、ネフシ、ケデマ、イシマエルの子孫は是の如し
Yeturi, Nafisi ndi Kedema. Awa anali ana a Ismaeli.
32 アブラハムの妾ケトラの生る子は左のごとし彼ジムラン、ヨクシヤン、メダン、ミデアン、イシバク、シユワを生りヨクシヤンの子等はシバおよびデダン
Ana a Ketura mzikazi wa Abrahamu anali awa: Zimurani, Yokisani, Medani, Midiyani, Isibaki ndi Suwa. Ana a Yokisani ndi awa: Seba ndi Dedani
33 ミデアンの子等はエバ、エペル、ヘノク、アビダ、エルダア是等はみなケトラの生る子なり
Ana aamuna a Midiyani anali, Efai, Eferi, Hanoki, Abida ndi Elida. Onsewa anali zidzukulu za Ketura.
34 アブラハム、イサクを生りイザクの子等はヱサウとイスラエル
Abrahamu anabereka Isake. Ana a Isake anali awa: Esau ndi Israeli.
35 エサウの子等はエリバズ、リウエル、ヱウシ、ヤラム、コラ
Ana aamuna a Esau anali awa: Elifazi, Reueli, Yeusi, Yolamu ndi Kora.
36 エリバズの子等はテマン、オマル、ゼビ、ガタム、ケナズ、テムナ、アマレク
Ana a Elifazi anali awa: Temani, Omari, Zefo, Gatamu ndi Kenazi: Amene anabereka ndi Timna: Amaleki.
37 リウエルの子等はナハテ、ゼラ、シヤンマ、ミツザ
Ana a Reueli anali awa: Nahati, Zera, Sama ndi Miza.
38 セイの子等はロタン、シヨバル、ヂベオン、アナ、デシヨン、エゼル、デシヤン
Ana a Seiri anali awa: Lotani, Sobala, Zibeoni, Ana, Disoni, Ezeri ndi Disani.
39 ロタンの子等はホリとホマム、ロタンの妹はテムナ
Ana aamuna a Lotani anali awa: Hori ndi Homamu. Timna anali mlongo wake wa Lotani.
40 シヨバルの子等はアルヤン、マナハテ、エバル、シピ、オナム、ヂベオンの子等はアヤとアナ
Ana aamuna a Sobala anali awa: Alivani, Manahati, Ebala, Sefo ndi Onamu. Ana aamuna a Zibeoni anali awa: Ayiwa ndi Ana.
41 アナの子等はデシヨン、デシヨンの子等はハムラム、エシバン、イテラン、ケラン、
Mwana wa Ana anali Disoni. Ana a Disoni anali awa: Hemudani, Esibani, Itirani ndi Kerani
42 エゼルの子等はビルハン、ザワン、ヤカン、デシヤンの子等はウズおよびアラン
Ana aamuna a Ezeri anali awa: Bilihani, Zaavani ndi Yaakani. Ana aamuna a Disani anali awa: Uzi ndi Arani.
43 イスラエルの子孫を治むる王いまだ有ざる前にエドムの地を治めたる王等は左のごとしベオルの子ベラその都城の名はデナバといふ
Awa ndi mafumu amene ankalamulira dziko la Edomu, mfumu iliyonse ya Israeli isanayambe kulamulira kumeneko: Bela mwana wa Beori, mzinda wake ankawutcha Dinihaba.
44 ベラ薨てボズラのゼラの子ヨバブこれに代りて王となり
Bela atamwalira, Yobabu mwana wa Zera wochokera ku Bozira analowa ufumu mʼmalo mwake.
45 ヨバブ薨てテマン人の地のホシヤムこれにかはりて王となり
Yobabu atamwalira, Husamu wochokera ku dziko la Atemani, analowa ufumu mʼmalo mwake.
46 ホシヤム薨てベダデの子ハダデこれにかはりて王となれり彼モアブの野にてミデアン人を撃りその都城の名はアビテといふ
Husamu atamwalira, Hadadi mwana wa Bedadi, amene anagonjetsa Amidiyani mʼdziko la Mowabu, analowa ufumu mʼmalo mwake. Mzinda wake unkatchedwa Aviti.
47 ハダデ薨てマスレカのサムラこれに代りて王となり
Hadadi atamwalira, Samila wochokera ku Masireka analowa ufumu mʼmalo mwake.
48 サムラ薨て河の旁なるレホボテのサウルこれに代りて王となり
Samila atamwalira, Sauli wochokera ku Rehoboti wa ku Mtsinje analowa ufumu mʼmalo mwake.
49 サウル薨てアクボルの子バアルハナンこれに代りて王となり
Sauli atamwalira, Baala-Hanani mwana wa Akibori analowa ufumu mʼmalo mwake.
50 バアルハナン薨てハダデこれにかはりて王となれりその都城の名はパイといふその妻はマテレデの女子にして名をメヘタベルといへりマテレデはメザハブの女なり
Pamene Baala-Hanani anamwalira, Hadadi analowa ufumu mʼmalo mwake. Mzinda wake unkatchedwa Pau, ndipo dzina la mkazi wake linali Mehatabeli mwana wa Matiredi, mwana wamkazi wa Me-Zahabu.
51 ハダデも薨たり/エドムの諸侯は左のごとし、テムナ侯アルヤ侯ヱテテ侯
Hadadi anamwaliranso. Mafumu a ku Edomu anali: Timna, Aliva, Yeteti,
52 アホリバマ侯エラ侯ピノン侯
Oholibama, Ela, Pinoni,
53 ケナズ侯テマン侯ミブザル侯
Kenazi, Temani, Mibezari,
54 マグデエル侯イラム侯エドムの諸侯は是のごとし
Magidieli ndi Iramu. Awa anali mafumu a ku Edomu.

< 歴代誌Ⅰ 1 >