< Salmos 121 >

1 Cântico dos degraus: Levanto meus olhos aos montes. De onde virá meu socorro?
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Ndikweza maso anga ku mapiri; kodi thandizo langa limachokera kuti?
2 Meu socorro [vem] do SENHOR, que fez os céus e a terra.
Thandizo langa limachokera kwa Yehova, wolenga kumwamba ndi dziko lapansi.
3 Ele não deixará o teu pé se abalar, nem cochilará o teu guardião.
Sadzalola kuti phazi lako literereke; Iye amene amakusunga sadzawodzera.
4 Eis que não cochilará nem dormirá o Guardião de Israel.
Taonani, Iye amene amasunga Israeli sadzawodzera kapena kugona.
5 O SENHOR é o teu guardião; o SENHOR é a sombra à tua direita.
Yehova ndiye amene amakusunga; Yehova ndiye mthunzi wako ku dzanja lako lamanja.
6 O sol não te ferirá durante o dia, nem a lua durante a noite.
Dzuwa silidzakupweteka nthawi ya masana, kapena mwezi nthawi ya usiku.
7 O SENHOR te guardará de todo mal; ele guardará a tua alma.
Yehova adzakuteteza ku zoyipa zonse; adzasunga moyo wako.
8 O SENHOR guardará tua saída e tua entrada, desde agora e para sempre.
Yehova adzayangʼanira kutuluka kwako ndi kulowa kwako; kuyambira tsopano mpaka muyaya.

< Salmos 121 >