< Neemias 4 >

1 Mas quando Sanballat ouviu que estávamos construindo o muro, ficou furioso, e ficou muito indignado, e zombou dos judeus.
Sanibalati atamva kuti tikumanganso khoma anapsa mtima nayamba kuseka ndi kunyogodola Ayuda kwambiri.
2 Ele falou diante de seus irmãos e do exército de Samaria, e disse: “O que esses judeus fracos estão fazendo? Será que eles se fortificarão? Será que eles vão se sacrificar? Será que vão terminar em um dia? Reanimarão as pedras dos montes de lixo, já que estão queimadas?”
Ndipo anayankhula pamaso pa abale ake ndi asilikali a Samariya kuti, “Kodi Ayuda ofowokawa akuchita chiyani? Kodi iwo nʼkumanganso khoma? Kodi adzaperekanso nsembe? Kodi adzatsiriza ntchitoyi tsiku limodzi? Kodi adzachita kutenga miyala yakale ija ndi mmene inapseramo?”
3 Now Tobias, o amonita, estava por ele, e disse: “O que eles estão construindo, se uma raposa subisse, ele derrubaria sua parede de pedra”.
Tobiya wa ku Amoni, amene anali naye anati, “Chimene akumangacho ngati nkhandwe itakwerapo, itha kugwetsa khoma lawolo!”
4 “Ouça, nosso Deus, pois somos desprezados. Voltem a repreender a sua própria cabeça. Desista deles por um saque em uma terra de cativeiro.
Tsono ndinayamba kupemphera kuti, “Timvereni, Inu Mulungu wathu, mmene akutinyozera. Mulole kuti mawu awo onyoza awabwerere, ndipo atengedwe ukapolo ku dziko lachilendo.
5 “Não cubra sua iniqüidade. Não deixe que o pecado deles seja apagado de diante de você; pois eles insultaram os construtores”.
Musawakhululukire mphulupulu zawo kapena kufafaniza machimo awo pamaso panu popeza aputa ukali wanu pamaso pa anthu omanga khoma.”
6 Assim, construímos o muro; e todo o muro foi unido à metade de sua altura, pois o povo tinha uma mente para trabalhar.
Choncho ife tinamangabe khomalo kufikira lonse litafika theka la msinkhu wake, chifukwa chakuti anthu anagwira ntchitoyo ndi mtima wawo wonse.
7 Mas quando Sambalate, Tobias, os árabes, os amonitas e os ashdoditas ouviram que o conserto dos muros de Jerusalém foi adiante e que as brechas começaram a ser preenchidas, ficaram muito irritados;
Koma pamene Sanibalati, Tobiya, Aarabu, Aamoni ndi anthu a ku Asidodi anamva kuti ntchito yokonzanso makoma a Yerusalemu ikupitirirabe ndipo kuti mipata ikutsekedwa, anapsa mtima kwambiri.
8 e todos eles conspiraram juntos para vir e lutar contra Jerusalém, e para causar confusão entre nós.
Tsono onse anapangana za chiwembu kuti abwere ndi kudzathira nkhondo anthu a ku Yerusalemu ndi kuyambitsa mapokoso pakati pawo.
9 Mas fizemos nossa oração ao nosso Deus, e colocamos uma vigília contra eles dia e noite por causa deles.
Koma ife tinapemphera kwa Mulungu wathu ndipo tinayika alonda otiteteza kwa adaniwo usiku ndi usana.
10 Judah disse: “A força dos carregadores de fardos está desaparecendo e há muitos escombros, de modo que não somos capazes de construir o muro”.
Pa nthawi yomweyi anthu a ku Yuda anati, “Mphamvu za anthu onyamula zinyalala zikutha ndipo pali zinyalala zambiri. Choncho ife sititha kumanga khomali.”
11 Nossos adversários disseram: “Eles não saberão ou verão, até que nós entremos no meio deles e os matemos, e façamos cessar o trabalho”.
Adani athunso anati, “Iwo asanadziwe izi, kapena kutiona, tidzakhala tili pakati pawo ndipo tidzawapha ndi kuyimitsa ntchitoyo.”
12 Quando os judeus que viviam por eles vieram, eles nos disseram dez vezes de todos os lugares: “Para onde quer que você se vire, eles nos atacarão”.
Ndipo Ayuda amene ankhala pafupi ndi adani athuwo anabwera kakhumi konse kuchokera konse kumene ankakhala kudzatiwuza kuti tibwereko ku ntchito.
13 Therefore Coloco guardas nas partes mais baixas do espaço atrás da parede, nos lugares abertos. Eu coloco as pessoas por grupos familiares com suas espadas, suas lanças e seus arcos.
Choncho kumbuyo kwa khoma, cha mʼmunsi mwake komanso malo amene anali asanathe ndinayikamo anthu mʼmabanja atatenga malupanga, mikondo ndi mauta awo.
14 Olhei, e me levantei, e disse aos nobres, aos governantes, e ao resto do povo: “Não tenham medo deles! Lembrem-se do Senhor, que é grande e impressionante, e lutem por seus irmãos, seus filhos, suas filhas, suas esposas e suas casas”.
Popeza anthu ankachita mantha, tsono ndinawawuza anthu olemekezeka, akuluakulu ndiponso anthu onse kuti, “Musawaope. Kumbukirani kuti Ambuye ndi wamkulu ndipo ndi woopsa. Choncho menyerani nkhondo abale anu, ana aamuna ndi aakazi, akazi anu ndi nyumba zanu.”
15 Quando nossos inimigos souberam que era do nosso conhecimento, e que Deus tinha levado seus conselhos a nada, todos nós voltamos à parede, todos ao seu trabalho.
Adani athu atamva kuti ife tadziwa za chiwembu chawo, anadziwanso kuti Yehova walepheretsa zimene ankafuna kutichita. Choncho tinabwerera aliyense ku ntchito yake yomanga khoma.
16 Daquele tempo em diante, metade dos meus servos fez o trabalho, e metade deles segurava as lanças, os escudos, os arcos e as capas de correio; e os governantes estavam atrás de toda a casa de Judá.
Kuyambira tsiku limenelo mpaka mʼtsogolo mwake, theka la antchito anga linkagwira ntchito, pamene theka linalo limatenga mikondo, zishango, mauta ndi kuvala malaya azitsulo. Akuluakulu ankalimbikitsa Ayuda onse
17 Aqueles que construíram o muro, e aqueles que carregaram fardos se carregaram; todos com uma de suas mãos faziam o trabalho, e com a outra segurava sua arma.
amene ankamanga khoma. Anthu onyamula zinyalala aja ankagwira ntchito ndi dzanja limodzi, dzanja linali atanyamula chida chankhondo.
18 Among os construtores, todos usavam sua espada ao seu lado, e assim construíram. Aquele que tocou a trombeta foi por mim.
Mʼmisiri aliyense ankamangirira lupanga lake mʼchiwuno mwake akamagwira ntchito. Koma munthu woyimba lipenga anali pambali panga nthawi zonse.
19 I disse aos nobres, e aos governantes e ao resto do povo: “A obra é grande e amplamente difundida, e estamos separados na parede, longe um do outro.
Ndipo ine ndinati kwa anthu olemekezeka ndi anthu ena onse, “Ntchitoyi ndi yayikulu ndipo ili padera lalikulu ndipo ifeyo takhala motayanatayana kwambiri pa khoma.
20 Wherever você ouve o som da trombeta, junte-se a nós”. Nosso Deus lutará por nós”.
Tsono kulikonse kumene muliko, mukamva kulira kwa lipenga bwerani mudzasonkhane kumene kuli ine kuno. Mulungu wathu adzatimenyera nkhondo.”
21 So nós fizemos o trabalho. Metade das pessoas seguraram as lanças desde a subida da manhã até o aparecimento das estrelas.
Choncho enafe tinapitiriza kugwira ntchito, pamene theka lina linkanyamula mikondo kuyambira mʼbandakucha mpaka nyenyezi zitaoneka.
22 Likewise ao mesmo tempo eu disse ao povo: “Que todos com seu servo se hospedem em Jerusalém, para que à noite possam ser nossos guardas, e possam trabalhar durante o dia”.
Pa nthawi imeneyo ndinawuzanso anthuwo kuti, “Aliyense pamodzi ndi wantchito wake agone mu Yerusalemu kuti tikhale ndi otilondera usiku ndi kuti masana tizigwira ntchito.”
23 So nem eu, nem meus irmãos, nem meus servos, nem os homens da guarda que me seguiram tiraram nossas roupas. Todos levaram sua arma para a água.
Choncho ine, anzanga, antchito anga, ndi anthu otiteteza amene ankanditsata panalibe ndi mmodzi yemwe anavula zovala zake pogona. Aliyense anasunga chida chake chankhondo pambali pake.

< Neemias 4 >