< Salmos 129 >

1 Cántico gradual. MUCHO me han angustiado desde mi juventud, puede decir ahora Israel;
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. “Andizunza kwambiri kuyambira ubwana wanga,” anene tsono Israeli;
2 Mucho me han angustiado desde mi juventud; mas no prevalecieron contra mí.
“Andizunza kwambiri kuyambira ubwana wanga, koma sanandipambane.
3 Sobre mis espaldas araron los aradores: hicieron largos surcos.
Anthu otipula analima pa msana panga ndipo anapangapo mizere yayitali:
4 Jehová es justo; cortó las coyundas de los impíos.
Koma Yehova ndi wolungama; Iye wandimasula ku zingwe za anthu oyipa.”
5 Serán avergonzados y vueltos atrás todos los que aborrecen á Sión.
Onse amene amadana ndi Ziyoni abwezedwe pambuyo mwamanyazi.
6 Serán como la hierba de los tejados, que se seca antes que crezca:
Akhale ngati udzu womera pa denga la nyumba, umene umafota usanakule;
7 De la cual no hinchió segador su mano, ni sus brazos el que hace gavillas.
sungadzaze manja a owumweta kapena manja a omanga mitolo.
8 Ni dijeron los que pasaban: Bendición de Jehová sea sobre vosotros; os bendecimos en el nombre de Jehová.
Odutsa pafupi asanene kuti, “Dalitso la Yehova lili pa inu; tikukudalitsani mʼdzina la Yehova.”

< Salmos 129 >