< Psaltaren 108 >

1 En sång, en psalm av David.
Nyimbo. Salimo la Davide. Mtima wanga ndi wokhazikika, Inu Mulungu; ndidzayimba nyimbo, inde ndidzayimba nyimbo zotamanda ndi moyo wanga wonse.
2 Mitt hjärta är frimodigt, o Gud, jag vill sjunga och lova; ja, så vill min ära.
Dzukani, zeze ndi pangwe! Ine ndidzadzutsa mʼbandakucha.
3 Vakna upp, psaltare och harpa; jag vill väcka morgonrodnaden.
Ndidzakutamandani Yehova, pakati pa anthu a mitundu ina; ndidzayimba za Inu pakati pa anthu a mitundu ina.
4 Jag vill tacka dig bland folken, HERREN, och lovsjunga dig bland folkslagen.
Pakuti chikondi chanu nʼchachikulu, kutalika kwake kuposa kumwamba; kukhulupirika kwanu kumafika mlengalenga.
5 Ty din nåd är stor ända uppöver himmelen, och din trofasthet allt upp till skyarna.
Kwezekani Inu Mulungu, kuposa mayiko akumwamba, ndipo ulemerero wanu uphimbe dziko lonse lapansi.
6 Upphöjd vare du, Gud, över himmelen, och över hela jorden sträcke sig din ära.
Tipulumutseni ndi kutithandiza ndi dzanja lanu lamanja kuti iwo amene mumawakonda apulumutsidwe.
7 På det att dina vänner må varda räddade, må du giva seger med din högra hand och bönhöra mig.
Mulungu wayankhula kuchokera ku malo ake opatulika: “Mwachipambano Ine ndidzagawa Sekemu ndipo ndidzayesa chigwa cha Sukoti.
8 Gud har talat i sin helgedom: »Jag skall triumfera, jag skall utskifta Sikem och skall avmäta Suckots dal.
Giliyadi ndi wanga, Manase ndi wanganso; Efereimu ndi chipewa changa chodzitetezera, Yuda ndi ndodo yanga yaufumu.
9 Mitt är Gilead, mitt är Manasse, Efraim är mitt huvuds värn,
Mowabu ndi mbale yanga yosambiramo ndidzaponya nsapato zanga pa Edomu; ndidzafuwula mopambana pa Filisitiya.”
10 Juda min härskarstav; Moab är mitt tvagningskärl, på Edom kastar jag min sko; över filistéernas land höjer jag jubelrop.»
Ndani adzandifikitsa ku mzinda wotetezedwa? Ndani adzanditsogolera ku Edomu?
11 Vem skall föra mig till den fasta staden, vem leder mig till Edom?
Kodi sindinu Mulungu, Inu amene mwatikana ndipo simuperekezanso magulu athu ankhondo?
12 Har icke du, o Gud, förkastat oss, så att du ej drager ut med våra härar, o Gud?
Tithandizeni ife kulimbana ndi mdani, pakuti thandizo la munthu ndi lopanda pake.
13 Giv oss hjälp mot ovännen; ty människors hjälp är fåfänglighet. Med Gud kunna vi göra mäktiga ting; han skall förtrampa våra ovänner. Se Ära i Ordförkl.
Chifukwa cha Mulungu wathu, ife tidzapeza chipambano, ndipo adzapondereza pansi adani athu.

< Psaltaren 108 >